Yeremiya 37:13 BL92

13 Pokhala iye m'cipinda ca Benjamini, kapitao wa alonda anali kumeneko, dzina lace Iriya, mwana wa Selemiya, mwana wa Hananiya; ndipo iye anamgwira Yeremiya mneneri, nati, Ulinkupandukira kwa Akasidi.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 37

Onani Yeremiya 37:13 nkhani