28 Mau a iwo akuthawa akupulumuka m'dziko la Babulo, kuti alalikire m'Ziyoni kubwezera cilango kwa Yehova Mulungu wathu, kubwezera cilango cifukwa ca Kacisi wace.
Werengani mutu wathunthu Yeremiya 50
Onani Yeremiya 50:28 nkhani