Habakuku 1:12 BL92

12 Si ndinu wacikhalire, Yehova Mulungu wanga, wopatulika wanga? sitidzafa. Yehova munamuikiratu kuti aweruzidwe; ndipo Inu, Thanthwe, munamkhazika kuti alangidwe.

Werengani mutu wathunthu Habakuku 1

Onani Habakuku 1:12 nkhani