Nahumu 1:12 BL92

12 Atero Yehova: Angakhale iwo ali ndi mphamvu yokwanira, nacuruka momwemo, koma momwemonso adzasalikidwa, ndipo iye adzapitiratu. Cinkana ndakuzunza iwe, sindidzakuzunzanso.

Werengani mutu wathunthu Nahumu 1

Onani Nahumu 1:12 nkhani