2 Yehova ndiye Mulungu wansanje, nabwezera cilango; Yehova ndiye wobwezera cilango, ndi waukali ndithu; Yehova ndiye wobwezera cilango oyambana naye, nasungira mkwiyo pa adani ace.
Werengani mutu wathunthu Nahumu 1
Onani Nahumu 1:2 nkhani