Nahumu 1:2 BL92

2 Yehova ndiye Mulungu wansanje, nabwezera cilango; Yehova ndiye wobwezera cilango, ndi waukali ndithu; Yehova ndiye wobwezera cilango oyambana naye, nasungira mkwiyo pa adani ace.

Werengani mutu wathunthu Nahumu 1

Onani Nahumu 1:2 nkhani