Nahumu 3:10 BL92

10 Koma iye anatengedwa, analowa ndende; ana ace a makanda anaphwanyika polekeza pace pa miseu yace yonse; ndi pa omveka ace anacita maere, ndi akulu ace onse anamangidwa maunyolo.

Werengani mutu wathunthu Nahumu 3

Onani Nahumu 3:10 nkhani