Zefaniya 3:19 BL92

19 Taonani, nthawi yomweyo ndidzacita nao onse akuzunza iwe; ndipo ndidzapulumutsa wotsimphinayo, ndi kusonkhanitsa wopitikitsidwayo; ndipo ndidzawaika akhale cilemekezo ndi dzina, iwo amene manyazi ao anali m'dziko lonse.

Werengani mutu wathunthu Zefaniya 3

Onani Zefaniya 3:19 nkhani