7 Ndinati, Zedi udzandiopa Ine, udzalola kulangizidwa, kuti pokhala pace pasaonongeke, monga mwa zonse ndamuikira; koma analawirira mamawa, nabvunditsa macitidwe ao onse.
Werengani mutu wathunthu Zefaniya 3
Onani Zefaniya 3:7 nkhani