Akolose 2:23 BL92

23 zimene ziri naotu manenedwe a nzeru m'kutumikira kwa cifuniro ca mwini wace, ndi kudzicepetsa, ndi kusalabadira thupi; koma ziribe mphamvu konse yakuletsa cikhutitso ca thupi.

Werengani mutu wathunthu Akolose 2

Onani Akolose 2:23 nkhani