Mika 7:9 BL92

9 Ndidzasenza mkwiyo wa Yehova, cifukwa ndamcimwira, mpaka andinenera mlandu wanga, ndi kundiweruzira mlandu wanga; adzanditurutsira kwa kuunika, ndipo ndidzapenya cilungamo cace.

Werengani mutu wathunthu Mika 7

Onani Mika 7:9 nkhani