Yona 3:7 BL92

7 Ndipo analalikira, nanena m'Nineve mwa lamulo la mfumu ndi nduna zace, ndi kuti, Ngakhale munthu kapena nyama, ngakhale ng'ombe kapena nkhosa, zisalawe kanthu, zisadye, zisamwe madzi;

Werengani mutu wathunthu Yona 3

Onani Yona 3:7 nkhani