Yona 3:6 BL92

6 Pakuti mau awa anafikira mfumu ya Nineve, ndipo Inanyamuka ku mpando wace wacifumu, nibvula copfunda cace, nipfunda ciguduli, nikhala m'mapulusa.

Werengani mutu wathunthu Yona 3

Onani Yona 3:6 nkhani