Yoweli 2:13 BL92

13 ndipo ng'ambani mitima yanu, si zobvala zanu ai; ndi kurembenukira kwa Yehova Mulungu wanu; pakuti Iye ndiye wacisomo, ndi wodzala cifundo, wosapsa mtima msanga, ndi wocuruka kukoma mtima, ndi woleka coipaco.

Werengani mutu wathunthu Yoweli 2

Onani Yoweli 2:13 nkhani