Yoweli 2:23 BL92

23 Mukondwere tsono, inu ana a Ziyoni, nimusekerere m'Yehova Mulungu wanu; pakuti adzayamba kukupatsani mvula yamyundo, monga mwa cilungamo cace; nakubvumbitsirani mvula, mvula yamyundo ndi yamasika mwezi woyamba.

Werengani mutu wathunthu Yoweli 2

Onani Yoweli 2:23 nkhani