Yoweli 2:5 BL92

5 Atumphako ngati mkokomo wa magareta pamwamba pa mapiri, ngati kulilima kwa malawi a moto akupsereza ziputu, ngati mtundu wamphamvu wa anthu ondandalikira nkhondo.

Werengani mutu wathunthu Yoweli 2

Onani Yoweli 2:5 nkhani