Yoweli 3:2 BL92

2 ndidzasonkhanitsa amitundu onse, ndi kutsikira nao ku cigwa ca Yosafati; ndipo ndidzaweruzana nao komweko za anthu anga, ndi colowa canga Israyeli, amene anawabalalitsa mwa amitundu, nagawa dziko langa,

Werengani mutu wathunthu Yoweli 3

Onani Yoweli 3:2 nkhani