1 Atesalonika 3:6 BL92

6 Koma tsopano pofika Timoteo kwathu kucokera kwa inu, ndi kutifotokozera mbiri yokoma ya cikhulupiriro ndi cikondano canu, ndi kuti mutikumbukila bwino masiku onse, pokhumba kutiona ife, monganso ire kukuonani inu;

Werengani mutu wathunthu 1 Atesalonika 3

Onani 1 Atesalonika 3:6 nkhani