2 Atesalonika 1:11 BL92

11 Kukatero tikupemphereraninso nthawi zonse, kuti Mulungu wathu akakuyeseni inu oyenera kuitanidwa kwanu, nakakwaniritse comkomera conse, ndi nchito ya cikhulupiriro mumphamvu;

Werengani mutu wathunthu 2 Atesalonika 1

Onani 2 Atesalonika 1:11 nkhani