2 Timoteo 1:9 BL92

9 amene anatipulumutsa ife, natiitana ife ndi maitanidwe oyera, si monga mwa nchito zathu, komatu monga mwa citsimikizo mtima ca iye yekha, ndi cisomo, copatsika kwa ife mwa Kristu Yesu zisanayambe nthawi zoyamba,

Werengani mutu wathunthu 2 Timoteo 1

Onani 2 Timoteo 1:9 nkhani