8 Ndipo monga momwe Yane ndi Yambre anatsutsana naye Mose, kotero iwonso atsutsana naco coonadi; ndiwo anthu obvunditsitsa mtima, osatsimikizidwa pacikhulupiriro.
Werengani mutu wathunthu 2 Timoteo 3
Onani 2 Timoteo 3:8 nkhani