Afilipi 4:18 BL92

18 Koma ndiri nazo zonse, ndipo ndisefukira; ndadzazidwa, popeza ndalandira kwa Epafrodito zija zidacokera kwanu, mnunkho wa pfungo labwino, nsembe yolandirika, yokondweretsa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Afilipi 4

Onani Afilipi 4:18 nkhani