Tito 1:7 BL92

7 Pakuti woyang'anira ayenera kukhala wopanda cirema, ngati mdindo wa Mulungu; wosati waliuma, wosapsa mtima msanga, wosati waciwawa, wopanda ndeu, wosati wa cisiriro conyansa;

Werengani mutu wathunthu Tito 1

Onani Tito 1:7 nkhani