Malaki 3:3 BL92

3 ndipo adzakhala pansi ndi kuyenga ndi kuyeretsa siliva, nadzayeretsa ana a Levi, nadzawayengetsa ngati golidi ndi siliva; pamenepo iwo adzapereka kwa Yehova zopereka m'cilungamo.

Werengani mutu wathunthu Malaki 3

Onani Malaki 3:3 nkhani