Malaki 3:7 BL92

7 Kuyambira masiku a makolo anu mwapambuka kuleka malemba anga osawasunga. Bwererani kudza kwa Ine, ndipo Ine ndidzabwerera kwa inu, ati Yehova wa makamu. Koma inu mukuti, Tibwerere motani?

Werengani mutu wathunthu Malaki 3

Onani Malaki 3:7 nkhani