13 Anyamata ananyamula mphero,Ana nakhumudwa posenza nkhuni.
14 Akulu adatha kuzipata,Anyamata naleka nyimbo zao.
15 Cimwemwe ca mtima wathu calekeka,Masewera athu asanduka maliro.
16 Korona wagwa pamutu pathu;Kalanga ife! pakuti tinacimwa.
17 Cifukwa ca ici mtima wathu ufoka,Cifukwa ca izi maso athu acita cimbuuzi;
18 Pa phiri la Ziyoni lopasukaloAnkhandwe ayendapo.
19 Inu, Yehova, mukhala cikhalire,Ndi mpando wanu wacifumu ku mibadwo mibadwo.