Mika 6:8 BL92

8 Iye anakuuza, munthuwe, comwe ciri cokoma; ndipo Yehova afunanji nawe koma kuti ucite colungama, ndi kukonda cifundo ndi kuyenda modzicepetsa ndi Mulungu wako?

Werengani mutu wathunthu Mika 6

Onani Mika 6:8 nkhani