Mika 7:1 BL92

1 Kalanga ine! pakuti ndikunga atapulula zipatso za m'mwamvu, atakunkha m'munda wamphesa; palibe mphesa zakudya; moyo wanga ukhumba nkhuyu yoyamba kupsa.

Werengani mutu wathunthu Mika 7

Onani Mika 7:1 nkhani