Yona 1:7 BL92

7 Ndipo anati yense kwa mnzace, Tiyeni ticite maere, kuti tidziwe coipa ici catigwera cifukwa ca yani. M'mwemo anacita maere, ndipo maere anagwera Yona.

Werengani mutu wathunthu Yona 1

Onani Yona 1:7 nkhani