5 Yehova pakati pace ali wolungama; sadzacita cosalungama, m'mawa ndi m'mawa aonetsera ciweruzo cace poyera, cosasowa kanthu; koma wosalungama sadziwa manyazi.
Werengani mutu wathunthu Zefaniya 3
Onani Zefaniya 3:5 nkhani