1 Atesalonika 4:1 BL92

1 Cotsalira tsono, abale, tikupemphani ndi kukudandaulirani mwa Ambuye Yesu, kuti, monga munalandira kwa ife mayendedwe okoma, muyenera kuyendanso ndi kukondweretsa Mulungu, monganso mumayenda, eurukani koposa momwemo.

Werengani mutu wathunthu 1 Atesalonika 4

Onani 1 Atesalonika 4:1 nkhani