1 Petro 3:18 BL92

18 Pakuti Kristunso adamva zowawa kamodzi, cifukwa ca macimo, wolungama m'malo mwa osalungama, kuti akatifikitse kwa Mulungu; wophedwatu m'thupi, koma woparsidwa moyo mumzimu;

Werengani mutu wathunthu 1 Petro 3

Onani 1 Petro 3:18 nkhani