17 Cifukwa yafika nthawi kuti ciweruziro ciyambe pa nyumba ya Mulungu; komangati ciyamba ndi ife, citsiriziro ca iwo osamvera Uthenga Wabwino wa Mulungu cidzakhala ciani?
Werengani mutu wathunthu 1 Petro 4
Onani 1 Petro 4:17 nkhani