1 Petro 5:10 BL92

10 Ndipo Mulungu wa cisomo conse, amene adakuitanani kulowa ulemerero wace wosatha mwa Kristu, mutamva zowawa kanthawi, adzafikitsa inu opanda cirema mwini wace, adzakhazikitsa, adzalimbikitsa inu.

Werengani mutu wathunthu 1 Petro 5

Onani 1 Petro 5:10 nkhani