1 Petro 5:12 BL92

12 Mwa Silvano, mbale wathu wokhulupirika monga ndimayesa, ndalembera kwa inu mwacidule, ndi kudandaulira, ndi kucita umboni, kuti cisomo coona ca Mulungu ndi ici; m'cimeneci muimemo.

Werengani mutu wathunthu 1 Petro 5

Onani 1 Petro 5:12 nkhani