18 Ana inu, ndi nthawi yorsirtza iyi; ndipo monga mudamva kuti wokana. Krisru akudza, ngakhale tsopano alipo okana Kristu ambiri; mwa ici tizindikira kuti ndi nthawi yotsirizira iyi.
Werengani mutu wathunthu 1 Yohane 2
Onani 1 Yohane 2:18 nkhani