25 Koma iye wakupenyerera m'lamulo langwiro, ndilo laufulu, natero cipenyerere, ameneyo, posakhala wakumva wakuiwala, komatu wakucita nchito, adzakhala wodala m'kucita kwace.
Werengani mutu wathunthu Yakobo 1
Onani Yakobo 1:25 nkhani