Malaki 2:15 BL92

15 Ndipo sanatero kodi wina womtsalira mzimu? Ndipo winayo anatero bwanji? Anatero pofuna mbeu ya Mulungu. Koma sungani mzimu wanu; ndipo asamcitire monyenga mkazi wa ubwana wace ndi mmodziyense.

Werengani mutu wathunthu Malaki 2

Onani Malaki 2:15 nkhani