Malaki 2:16 BL92

16 Pakuti ndidana nako kuleka kumene, ati Yehova Mulungu wa Israyeli, ndi iye wakukuta cobvala cace ndi ciwawa, ati Yehova wa makamu; cifukwa cace sungani mzimu wanu kuti musacite mosakhulupirika.

Werengani mutu wathunthu Malaki 2

Onani Malaki 2:16 nkhani