1 Timoteo 3:16 BL92

16 Ndipo pobvomerezeka, cinsinsi ca kucitira Mulungu ulemu ncacikuru: iye amene anaonekera m'thupi, anayesedwa wolungama mumzimu, anapenyeka ndi angelo, analalikidwa mwa amitundu, wokhulupiridwa m'dziko lapansi, wolandiridwa m'ulemerero.

Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 3

Onani 1 Timoteo 3:16 nkhani