1 Timoteo 5:21 BL92

21 Ndikucitira umboni pamaso pa Mulungu, ndi Kristu Yesu, ndi angelo osankhika, kuti usunge izi kopanda kusankhiratu, wosacita kanthu monga mwa tsankhu.

Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 5

Onani 1 Timoteo 5:21 nkhani