Yakobo 4:4 BL92

4 Akazi acigololo inu, kodi simudziwa kuti ubwenzi wa dziko lapansi uti udani ndi Mulungu? Potero, iye amene afuna kukhala bwenzi la dziko lapansi adziika mdani wa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Yakobo 4

Onani Yakobo 4:4 nkhani