1 Timoteo 1:16 BL92

16 komatu mwa ici anandicitira cifundo, kuti mwa ine, woyamba, Yesu Kristu akaonetsere kuleza mtima kwace konse kukhale citsanzo ca kwa iwo adzakhulupirira pa iye m'tsogolo kufikira moyo wosatha.

Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 1

Onani 1 Timoteo 1:16 nkhani