16 amene iye yekha ali nao moyo wosatha, wakukhala m'kuunika kosakhozeka kufikako; amene munthu sanamuona, kapena sakhoza kumuona; kwa iye kukhale ulemu ndi mphamvu yosatha. Amen.
Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 6
Onani 1 Timoteo 6:16 nkhani