Ezara 1:1 BL92

1 CAKA coyamba tsono ca Koresi mfumu ya ku Perisiya, kuti akwaniridwe mau a Yehova m'kamwa mwa Yeremiya, Yehova anautsa mzimu wa Koresi, kuti abukitse mau m'ufumu wace wonse, nawalembenso, ndi kuti,

Werengani mutu wathunthu Ezara 1

Onani Ezara 1:1 nkhani