14 Ana a Bigivai, zikwi ziwiri mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi.
15 Ana a Adini, mazana anai mphambu makumi asanu kudza anai.
16 Ana a Ateri, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai mphambu asanu ndi atatu.
17 Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza atatu.
18 Ana a Yora, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.
19 Ana a Hasumu, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.
20 Ana a Gibara, makumi asanu ndi anai mphambu asanu.