17 Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza atatu.
18 Ana a Yora, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.
19 Ana a Hasumu, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.
20 Ana a Gibara, makumi asanu ndi anai mphambu asanu.
21 Ana a Betelehemu zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.
22 Anthu a ku Netofa, makumi asanu mphambu asanu ndi mmodzi.
23 Anthu a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.