35 Ana a Senai, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.
36 Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.
37 Ana a lmneri, cikwi cimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.
38 Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.
39 Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.
40 Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyeli, ndiwo a ana a Hodariya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.
41 Oyimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.