Ezara 3:9 BL92

9 Pamenepo anaimirira pamodzi Yesuwa ndi ana ace ndi abale ace, Kadimiyeli ndi ana ace, ana a Yuda, kuyang'anira ogwira nchito m'nyumba ya Yehova, ana a Henadadi ndi ana ao ndi abale ao Alevi.

Werengani mutu wathunthu Ezara 3

Onani Ezara 3:9 nkhani