Ezara 5:11 BL92

11 Natiyankha mau motere, ndi kuti, Ife ndife akapolo a Mulungu wa Kumwamba ndi dziko lapansi, tirikumanga nyumba imene idamangika zapita zaka zambiri; inaimanga ndi kuitsiriza mfumu yaikuru ya Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezara 5

Onani Ezara 5:11 nkhani