1 Zitatha izi tsono, pokhala mfumu Aritasasta mfumu ya Perisiya, anadza Ezara mwana wa Seraya, mwana wa Azariya, mwana wa Hilikiya,
2 mwana wa Salumu, mwana wa Zadoki, mwana wa Ahitubu,
3 mwana wa Amariya, mwana wa Azariya, mwana wa Meraioti,
4 mwana wa Zerahiya, mwana wa Uzi, mwana wa Buki,
5 mwana wa Abisuwa mwana wa Pinehasi, mwana wa Eleazara, mwana wa Aroni wansembe wamkuru.